Posts

Showing posts from July, 2024

TIDIKIRE MPAKA AYAKE - CHIFUKWA IZI NDIYE NDI KHWESI

Image
 Anthu  ambiri ochita malonda anali kakasi kaamba ka kuzima kwa magetsi komwe kunachitika masana a lachiwiri  pa 9 July. Vuto la kuzima kwa magetsili  linasokoneza ntchito zamalonda, maka zomwe zimadalira magetsi mmadera ambiri m'boma la Lilongwe. Mwachitsazo, pa msika waung'ono  wa Matindi, achinyamata omwe amachita bizinezi yometa anthu komanso kutchaja mafoni adandaula kuti vuto la kuzima kwa magetsili lasokoneza kwambiri ntchito zawo lero.  Nawo amayi omwe amafuna kukagayitsa, anali khumakhuma mmakonde a zigayo kudikira kuti mwina magetsiwa  ayaka. Ndipotu ngakhale kuti kunja kunali kutada, Nathenje Community Radio inapeza amayi ochuluka omwe anali  akudikirabe  mmakonde azigayozi poganiza kuti mwina magetsiwa ayaka. Ndipo patatha maola oposa asanu ndi limodzi kuchokera pomwe magetsiwa athima, Magetsi anayaka.  Chomwe chinachititsa kuti magetsiwa azime motere sichikudziwika pakali pano. Wolemba: Enerst M Manyoni

AONESA CHIDWI CHODZAPIKISANA NAWO NGATI KHASALA

Image
  Modzi mwa achinyamata okhala pa Nathenje  Gift Mkochi watsimikiza kuti ayimira nawo ngati Khasala wa Ngala Ward pachisankho chomwe chichitike chaka cha mawa dziko muno. a Mkochi ati akufuna kudzapikisana nawo pa chisankhochi atawona kuti kwanthawi yayitali Ngala Ward yatsalira Ku nkhani ya chitukuko.  "Inetu ndi mwana wamudzi muno, ndaphunzira konkuno ndipo zanga zonse zili kuno. Ndi zokhumudwitsa kuti ntchito ya Khasala kwathu kuno sikudziwika!!! Ndikufuna anthu adziwe kuti Khasala amatani" anayakhula motero a Mkochi Iwoso atsimikiza kuti akonzeka kukathamangitsana ndi anzawo ena kumasankho achipulura a chipani cha Malawi Kongelesi mwezi wa seputembala uno Wolemba: Alinafe Jonasi & Loveness Chiutsi Chithunzi: Shadow Khasala Gift Mkochi

"MUSICIAN GIBOH PEARSON ESCAPES DEATH IN TERRIFYING CAR ACCIDENT

Image
Renowned musician Giboh Pearson survived a harrowing car accident earlier on 8th July 2024, escaping without injuries. The talented artist took to his Facebook page to share the shocking news, revealing that the incident occurred while he was en route to a music festival in Bangwe, following a performance in Zomba. According to Pearson, the vehicle's steering and brakes failed, causing the car to overturn. Miraculously, no one was hurt in the accident. The musician expressed his gratitude for the narrow escape, acknowledging the severity of the situation. Pearson's fans and well-wishers have flooded his Facebook post with relief and support, thanking God for his safety. The musician's close call serves as a poignant reminder of the fragility of life and the importance of cherishing every moment. Despite the scare, Pearson remains committed to his craft, with fans eagerly anticipating his next performance. Reported by Aspolo Mousah

CASTLE OF DREAMERS SET TO EMBRACE POSITIVE CHANGE.

Image
A newly born local non-profit organization called Castle of Dreamers has unveiled its concept to unemployed youth from various higher learning institutions, focusing on providing them with hands-on working experience. Speaking on Sunday the 14th May 2024 during a colorful event which was held at IMPACT Gardens in Nathenje, the main speaker, Franklin Chilomba, stated that the organization aims to bridge the gap between new graduates and potential employers. Chilomba observes that for decades, the experience requirement demanded by employers has been a barrier for recent university graduates in securing jobs. Chilomba adds that he is optimistic that this initiative will result in more youth finding employment after acquiring skills from experienced professionals and gaining hands-on experience. He states that internship programs for these youths, who have expressed interest in areas such as Sustainable Agriculture, Health, Education, Water and Sanitation, Journalism, Community Developmen...

AFTER DEADLY PROTESTS, KENYANS TELL OF BRUTAL ABDUCTIONS

Image
Dozens of activists say they were snatched from their homes or off the streets by hooded, armed men. Some are still missing, and the disappearances have unnerved a nation long seen as a pillar of stability. One activist was taken while organizing a blood drive for wounded protesters. Another said he was snatched as he worked at home after midnight, his wife and three children sleeping nearby. A third said he was beaten and blindfolded before being tossed into the trunk of a car. All of them said they were swept up by government security forces in Kenya over the past two weeks after they had spoken out against a contentious bill to raise taxes in the cash-strapped East African nation. Some had participated in the wave of antigovernment protests that rocked Kenya after the bill was first introduced. At least 39 people were killed during clashes with the police in June, according to the Kenya National Commission on Human Rights. At least 32 people, including activists, medical workers and...